Danieli 2:41 BL92

41 Ndipo umo mudaonera mapazi ndi zala zace, mwina dongo la woumba, mwina citsulo; ufumuwo udzakhala wogawanika, koma momwemo mudzakhala mphamvu ya citsulo; popeza mudaona citsulo cosanganizika ndi dongo.

Werengani mutu wathunthu Danieli 2

Onani Danieli 2:41 nkhani