Danieli 6:24 BL92

24 Ndipo italamulira mfumu, anabwera nao amuna aja adamneneza Danieli, nawaponya m'dzenje la mikango, iwowa, ana ao, ndi akazi ao; ndipo asanafike pansi pa dzenje mikango inawaposa mphamvu, niphwanya mafupa ao onse.

Werengani mutu wathunthu Danieli 6

Onani Danieli 6:24 nkhani