Danieli 6:3 BL92

3 Pamenepo Danieli amene anaposa akuluwa ndi akalonga, popeza munali mzimu wopambana mwa iye, ndi mfumu inati imuike woyang'anira ufumu wonse.

Werengani mutu wathunthu Danieli 6

Onani Danieli 6:3 nkhani