10 Ndi Yesuwa anabala Yoyakimu, ndi Yoyakimu anabala Eliasibi ndi Eliasibi anabala Yoyada,
11 ndi Yoyada anabala Yonatani, ndi Yonatani, anabala Yaduwa.
12 Ndi m'masiku a Yoyakimu ansembe akulu a nyumba za makolo ndiwo: wa Seraya, Meraya; wa Yeremiya, Hananiya;
13 wa Ezara, Mesulamu; wa Amariya, Yehohanana;
14 wa Maluki, Yonatani; wa Sebaniya, Yosefe;
15 wa Harimu, Adina; wa Merayoti, Helikai;
16 wa Ido, Zekariya; wa Ginetoni, Mesulamu;