12 Ndi m'masiku a Yoyakimu ansembe akulu a nyumba za makolo ndiwo: wa Seraya, Meraya; wa Yeremiya, Hananiya;
13 wa Ezara, Mesulamu; wa Amariya, Yehohanana;
14 wa Maluki, Yonatani; wa Sebaniya, Yosefe;
15 wa Harimu, Adina; wa Merayoti, Helikai;
16 wa Ido, Zekariya; wa Ginetoni, Mesulamu;
17 wa Abiya, Zikiri; wa Minyamini, wa Moadiya, Pilitai;
18 wa Biliga, Samura; wa Semaya, Yehonatani;