4 Ido, Ginetoi, Abiya,
5 Miyamini, Maadiya, Biliga,
6 Semaya, ndi Yoyaribi, Yedaya,
7 Salu, Amoki, Hilikiya, Yedaya. Awa ndi akuru a ansembe ndi abale ao m'masiku a Yesuwa.
8 Ndi Alevi ndiwo Yesuwa, Binui, Kadimiyeli, Serebiya, Yuda, ndi Mataniya; iye ndi abale ace amatsogolera mayamiko.
9 Ndi Bakibukiya ndi Uni, abale ao, anawayang'anira maulonda.
10 Ndi Yesuwa anabala Yoyakimu, ndi Yoyakimu anabala Eliasibi ndi Eliasibi anabala Yoyada,