9 Ndi Bakibukiya ndi Uni, abale ao, anawayang'anira maulonda.
10 Ndi Yesuwa anabala Yoyakimu, ndi Yoyakimu anabala Eliasibi ndi Eliasibi anabala Yoyada,
11 ndi Yoyada anabala Yonatani, ndi Yonatani, anabala Yaduwa.
12 Ndi m'masiku a Yoyakimu ansembe akulu a nyumba za makolo ndiwo: wa Seraya, Meraya; wa Yeremiya, Hananiya;
13 wa Ezara, Mesulamu; wa Amariya, Yehohanana;
14 wa Maluki, Yonatani; wa Sebaniya, Yosefe;
15 wa Harimu, Adina; wa Merayoti, Helikai;