Nehemiya 2:3 BL92

3 Ndipo ndinati kwa mfumu, Mfumu ikhale ndi moyo kosatha; ilekerenji nkhope yanga kucita cisoni, popeza pali bwinja kumudzi kuli manda a makolo anga, ndi zipata zace zopsereza ndi moto.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 2

Onani Nehemiya 2:3 nkhani