Nehemiya 6:7 BL92

7 Ndiponso waika aneneri akubukitsa za iwe ku Yerusalemu, ndi kuti, Ku Yuda kuli mfumu, ndipo zidzamveka kwa mfumu, kuti kuli zotere. Tiyeni tsono tipangane pamodzi.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 6

Onani Nehemiya 6:7 nkhani