41 Ana a Pasuru, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi anai ndi asanu ndi awiri.
42 Ana a Harimu, cikwi cimodzi mphambu khumi limodzi kudza asanu ndi awiri.
43 A Levi: ana a Yesuwa, a Kadimiyeli, a ana a Hodeva, makumi asanu ndi awiri kudza anai.
44 Oyimbira: ana a Asafu, zana limodzi mphambu makumi anai kudza asanu ndi atatu.
45 Odikira: ana a Salumu, ana a Ateri, ana a Talimoni, ana a Akubu, ana a Hatita, ana a Sobai, zana limodzi mphambu makumi atatu kudza asanu ndi atatu.
46 Anetini: ana a Ziha, ana a Hasufa, ana a Tabaoti,
47 ana a Kerosi, ana a Siya, ana a Padoni,