8 ana a Parosi zikwi ziwiri mphambu zana limodzi kudza makumi asanu ndi awiri.
9 Ana a Sefatiya, mazana atatu mphambu makumi asanu ndi awiri kudza awiri.
10 Ana a Ara, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu kudza awiri.
11 Ana a Pakati Moabu, a ana a Yesuwa ndi Yoabu, zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi atatu kudza khumi limodzi ndi asanu ndi atatu.
12 Ana a Elamu, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri ndi makumi asanu kudza anai.
13 Ana a Zatu, mazana asanu ndi atatu mphambu makumi anai kudza asanu.
14 Ana a Zakai, mazana asanu ndi awiri mphambu makumi asanu ndi limodzi.