Nehemiya 8:2 BL92

2 Ndipo Ezara wansembe anabwera naco cilamulo pamaso pa msonkhano, ndiwo amuna ndi akazi, ndi yense wakumva ndi kuzindikira tsiku loyamba la mwezi wacisanu ndi ciwiri.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 8

Onani Nehemiya 8:2 nkhani