13 Munatsikiranso pa phiri la Sinai, nimunalankhula nao mocokera m'Mwamba, ndipo munawapatsa maweruzo oyenera, ndi cilamulo coona, malemba, ndi malamulo okoma;
Werengani mutu wathunthu Nehemiya 9
Onani Nehemiya 9:13 nkhani