Nehemiya 9:37 BL92

37 Ndipo licurukitsira mafumu zipatso zace, ndiwo amene munawaika atiweruze, cifukwa ca zoipa zathu; acitanso ufumu pa matupi athu, ndi pa zaweta zathu, monga umo akonda; ndipo ife tisauka kwakukuru.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 9

Onani Nehemiya 9:37 nkhani