2 Akorinto 11:20 BL92

20 Pakuti mulola ngati wina akuyesani inu akapolo, ngati wina alikwira inu, ngati wina alanda zanu, ngati wina adzikuza, ngati wina akupandani pankhope.

Werengani mutu wathunthu 2 Akorinto 11

Onani 2 Akorinto 11:20 nkhani