2 Akorinto 12:2 BL92

2 Ndidziwa munthu wa mwa Kristu, zitapita zaka khumi ndi zinai (ngati m'thupi, sindidziwa; ngati kunja kwa thupi, sindidziwa; adziwa Mulungu), anakwatulidwa wotereyo kunka naye Kumwamba kwacitatu.

Werengani mutu wathunthu 2 Akorinto 12

Onani 2 Akorinto 12:2 nkhani