2 koma takaniza zobisfka za manyazi, osayendayenda mocenjerera, kapena kucita nao mau a Mulungu konyenga; koma ndi maonekedwe a coonadi tidzibvomeretsa tokha ku cikumbu mtima ca anthu onse pamaso pa Mulungu.
Werengani mutu wathunthu 2 Akorinto 4
Onani 2 Akorinto 4:2 nkhani