2 Akorinto 7:14 BL92

14 Pakuti ngati ndadzitamandira nako kanthu kwa iye cifukwa ca inu, sindinamvetsedwa manyazi; koma monga tinalankhula zonse ndi inu m'coonadi, koteronso kudzitamandira kwathu kumene kwa Tito, kunakhala coonadi.

Werengani mutu wathunthu 2 Akorinto 7

Onani 2 Akorinto 7:14 nkhani