Nehemiya 10:39 BL92

39 Pakuti ana a Israyeli ndi ana a Levi, azibwera nayo nsembe yokweza yatirigu, ndi yavinyo ndi yamafuta, kuzipinda kuli zipangizo za malo opatulika, ndi ansembe akutumikira, ndi odikira, ndi oyimbira; kuti tisasiye nyumba ya Mulungu wathu.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 10

Onani Nehemiya 10:39 nkhani