36 Ana a Yeriko, mazana atatu mphambu makumi anai kudza asanu.
37 Ana a Lodi, Hadidi, ndi Ono, mazana asanu ndi awiri mphambu makumi awiri kudza mmodzi.
38 Ana a Senaa, zikwi zitatu mphambu mazana asanu ndi anai kudza makumi atatu.
39 Ansembe: ana a Yedaya, a nyumba ya Yesuwa, mazana asanu ndi anai mphambu makumi asanu ndi awiri kudza atatu.
40 Ana a Imeri, cikwi cimodzi mphambu makumi asanu kudza awiri.
41 Ana a Pasuru, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi anai ndi asanu ndi awiri.
42 Ana a Harimu, cikwi cimodzi mphambu khumi limodzi kudza asanu ndi awiri.