Nehemiya 7:67 BL92

67 osawerenga akapolo ao amuna ndi akazi, ndiwo zikwi zisanu ndi ziwiri mphambu mazana atatu ndi makumi atatu kudza asanu ndi awiri; ndipo anakhala nao amuna ndi akazi oyimbira mazana awiri mphambu makumi anai kudza asanu ndi mmodzi.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 7

Onani Nehemiya 7:67 nkhani