1 Tsatani cikondi; koma funitsitsani mphatsozauzimu, koma koposa kuti mukanenere.
2 Pakuti iye wakulankhula lilime salankhula ndi anthu, koma ndi Mulungu; pakuti palibemunthu akumva; koma mumzimu alankhula zinsinsi.
3 Koma iye wakunenera alankhula ndi anthu comangirira ndi colimbikitsa, ndi cosangalatsa,
4 Iye wakulankhula lilime, adzimangirira yekha, koma iye wakunenera amangirira Mpingo.