34 Akazi akhale cete m'Mipingo. Pakuti vsikuloledwa kwa iwo kulankhula, Koma akhale omvera, mongansocilamulo cmena,
35 Koma ngati afuna kuphunzirakanthu afunseamuna ao aiwo okha kwao; pakuti kunyazitsa mkazi kulankhula mu Mpingo.
36 Kodi mau a Mulungu anatutuka kwa iw? kapena anafika kwa inu nokha?
37 Ngatiwinaayesa kuti ali mneneri, kapena wauzimu; azindikire kuti zimene ndilemba kwa inu ziri lamulo la Ambuye,
38 Koma ngati wina akhale wosadziwa, akhale wosadziwa.
39 Cifukwa cace; abale anga, funitsitsani kunenera, ndipo musaletse kulankhula malilime.
40 Koma zonse zicitike koyenera ndi kolongosoka.