19 Pakuti nzeru ya dziko ina lapansi iri yopusa kwa Mulungu, Pakuti, kwalembedwa, iye agwira mzeru m'cenjerero lao;
20 ndiponso Ambuye azindikira zolingirira za mzeru, kuti ziri zopanda pace.
21 Cifukwa cace palibemmodzi adziamande mwa anthu. Pakuti zinthu onse nzanu;
22 ngati Paulo, kapena Apolo, kapena Kefa, kapena dziko apansi, kapena moyo, kapena imfa, capena za makono ano, kapena drinkudza; zonse ndi zanu;
23 kona inu ndinu a Kristu; ndi Kristu ndiye wa Mulungu.