1 Akorinto 4:15 BL92

15 Pakuti mungakhale muli nao aphunzitsi zikwi khumi mwa Kristu, mulibe atate ambiri; pakuti mwa Kristu Yesu ine ndinabala Inu mwa Uthenga Wabwino.

Werengani mutu wathunthu 1 Akorinto 4

Onani 1 Akorinto 4:15 nkhani