1 Akorinto 4:17 BL92

17 Cifukwa ca ici ndatuma kwa inu Timoteo, ndiye mwana wanga wokondedwa ndi wokhulupirika mwa Ambuye, amene adzakumbutsa inu njira zanga za mwa Kristu, monga ndiphunzitsa ponsepom'Mipingo yonse.

Werengani mutu wathunthu 1 Akorinto 4

Onani 1 Akorinto 4:17 nkhani