36 Koma wina akayesa kuti acitira mwana wace wamkazi cosamuyeoera, ngati palikupitirira pa unamwali wace, ndipo kukafunika kutero, acite cimene afuna, sacimwa; akwatitsidwe.
Werengani mutu wathunthu 1 Akorinto 7
Onani 1 Akorinto 7:36 nkhani