2 Akorinto 11:4 BL92

4 Pakutitu ngati iye wakudza alalikira Yesu wina, amene ife sitinalalikira, kapena ngati mulandira mzimu wa mtundu wina, umene simunalandira, kapena uthenga wabwino wa mtundu wina umene simunalandira, mulolana nave bwino lomwe.

Werengani mutu wathunthu 2 Akorinto 11

Onani 2 Akorinto 11:4 nkhani