Nehemiya 2:19 BL92

19 Koma Sanibalati Mhoroni, ndi Tobiya kapolo M-amoniyo, ndi Gesemu M-arabu, anamva natiseka pwepwete, natipeputsa, nati, Ciani ici mucicita? Mulikupandukira mfumu kodi?

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 2

Onani Nehemiya 2:19 nkhani