Nehemiya 8:13 BL92

13 Ndipo m'mawa mwace akuru a nyumba za makolo a anthu onse, ansembe, ndi Alevi anasonkhana pamodzi kwa Ezara mlembi, kuti atole nzeru za mau a cilamulo.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 8

Onani Nehemiya 8:13 nkhani