18 Koma ena adzitukumula, monga ngati sindinalinkudza kwa inu.
19 Koma ndidzafika kwa inu msanga, akandilola Ambuye; ndipo ndidzazindikira si mau a iwo odzitukumula, koma mphamvuyi.
20 Pakuti ufumu wa Mulungu suli m'mau, koma mumphamvu, Mufuna ciani?
21 Kodi ndifike kwa inu ndi ndodo, kapena mwacikondi, ndi mzimu wakufatsa?