1 Akorinto 9:7 BL92

7 Msilikari ndani acita nkhondo, nthawi iriyonse, nadzifunira zace yekha? Aoka mipesa ndani, osadya cipatso cace? Kapena aweta gulu ndani, osadyamkaka wace wa gululo? Kodi ndilankhula izi monga mwa anthu?

Werengani mutu wathunthu 1 Akorinto 9

Onani 1 Akorinto 9:7 nkhani