2 Akorinto 11:2 BL92

2 Pakuti ndicita nsanje pa inu ndi nsanje ya Mulungu; pakuti ndinakupalitsani ubwenzi mwamuna mmodzi, kuti ndikalangize inu ngati namwali woyera mtima kwa Kristu.

Werengani mutu wathunthu 2 Akorinto 11

Onani 2 Akorinto 11:2 nkhani