18 Ngati nkutheka, monga momwe mukhoza, khalani ndi mtendere ndi anthu onse.
19 Musabwezere coipa, okondedwa, koma patukani pamkwiyo; pakuti kwalembedwa, Kubwezera kuli kwanga, Ine ndidzabwezera, ati Ambuye.
20 Koma ngati mdani wako akumva njala, umdyetse, ngati akumva ludzu, ummwetse; pakuti pakutero udzaunjika makala a mota pamutu pace.
21 Musagonje kwa coipa, koma ndi cabwino genietsani coipa.