Aroma 7:13 BL92

13 Ndipo tsopano cabwino cija cinandikhalira imfa kodi? Msatero ai. Koma ucimo, kuti uoneke kuti uli ucimo, wandicitira imfa mwa cabwino cija; kuti ucimo ukakhale wocimwitsa ndithu mwa lamulo.

Werengani mutu wathunthu Aroma 7

Onani Aroma 7:13 nkhani