Aroma 8:11 BL92

11 Koma ngati Mzimu wa iye amene adaukitsa Yesu kwa akufa akhalabe mwa inu, iye amene adaukitsa Kristu Yesu kwa akufa adzapatsanso moyo matupi anu akufa, mwa Mzimu wace wakukhala mwa inu.

Werengani mutu wathunthu Aroma 8

Onani Aroma 8:11 nkhani