Aroma 8:34 BL92

34 9 ndani adzawatsutsa? Kristu Yesu ndiye amene adafera, inde makamaka, ndiye amene adauka kwa akufa, 10 amene akhalanso pa dzanja lamanja la Mulungu, 11 amenenso atipempherera ife.

Werengani mutu wathunthu Aroma 8

Onani Aroma 8:34 nkhani