Marko 1:27 BL92

27 Ndipo anazizwa onse, kotero kuti anafunsana mwa iwo okha, kuti, Ici nciani? ciphunzitso catsopano! ndi mphamvu alamula ingakhale mizimu yonyansa, ndipo imvera Iye.

Werengani mutu wathunthu Marko 1

Onani Marko 1:27 nkhani