Marko 10:24 BL92

24 Ndipo ophunzirawo anazizwa ndithu ndi mau ace. Koma Yesu anayankhanso nanena nao, Ananu, nkobvuta ndithu kwa iwo akutama cuma kulowa mu Ufumu wa Mulungu!

Werengani mutu wathunthu Marko 10

Onani Marko 10:24 nkhani