Marko 15:43 BL92

43 anadzapo Y osefe wa ku Arimateya, mkulu wa mirandu womveka, amene yekha analikuyembekezera Ufumu wa Mulungu; nalimba mtima nalowa kwa Pilato, napempha mtembo wace wa Yesu.

Werengani mutu wathunthu Marko 15

Onani Marko 15:43 nkhani