Marko 7:24 BL92

24 Ndipo Iye anauka nacoka kumeneko, nanka ku maiko a ku Turo ndi Sidoni, Ndipo analowa m'nyumba, nafuna kuti asadziwe anthu; ndipo sanakhoza kubisika.

Werengani mutu wathunthu Marko 7

Onani Marko 7:24 nkhani