Marko 8:17 BL92

17 Ndipo Yesu pamene anazindikira, ananena nao, Bwanji mutsutsana cifukwa mulibe mkate? kodi kufikira tsopano simuzindikira, nisimudziwitsa? kodi muli nayo mitima yanu youma?

Werengani mutu wathunthu Marko 8

Onani Marko 8:17 nkhani