Marko 8:33 BL92

33 Koma Iye anapotoloka, napenya ophunzira ace, namdzudzula Petro, nanena, Coka, pita kumbuyo kwanga, Satana iwe; popeza susamalira zinthu za Mulungu, koma za anthu.

Werengani mutu wathunthu Marko 8

Onani Marko 8:33 nkhani