Marko 9:1 BL92

1 Ndipo ananena nao, Ndithu ndinena ndi inu kuti, Alipo ena akuimirira pano, amene sadzalawa imfa konse, kufikira akaona Ufumu wa Mulungu utadza ndi mphamvu.

Werengani mutu wathunthu Marko 9

Onani Marko 9:1 nkhani