Marko 9:31 BL92

31 Pakuti anaphunzitsa ophunzira ace, nanena nao, kuti, Mwana wa munthu aperekedwa m'manja a anthu, ndipo adzamupha Iye; ndipo ataphedwa, adzauka pofika masiku atatu.

Werengani mutu wathunthu Marko 9

Onani Marko 9:31 nkhani