Marko 9:41 BL92

41 Pakuti munthu ali yense adzakumwetsani inu cikho ca madzi m'dzina langa cifukwa muli ace a Kristu, indetu ndinena ndi inu, kuti iye sadzataya konse mphotho yace.

Werengani mutu wathunthu Marko 9

Onani Marko 9:41 nkhani