2 Samueli 1:16 BL92

16 Koma asanafe, Davide adanena naye, Wadziphetsa ndi mtima wako; cifukwa pakamwa pako padacita umboni wakukutsutsa ndi kuti, Ine ndinapha wodzozedwa wa Yehova.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 1

Onani 2 Samueli 1:16 nkhani