2 Samueli 13:13 BL92

13 Ndipo ine, manyazi anga ndidzapita nao kuti? ndipo iwenso udzakhala ngati wina wa zitsiru m'Israyeli. Cifukwa cace tsono ulankhule ndi mfumu; iyeyu sadzakukaniza ine.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 13

Onani 2 Samueli 13:13 nkhani