2 Samueli 13:31 BL92

31 Pamenepo mfumu inanyamuka ning'amba zobvala zace nigona pansi, ndipo anyamata ace onse anaimirirapo ndi zobvala zao zong'ambika.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 13

Onani 2 Samueli 13:31 nkhani