18 Ndipo anyamata ace onse anapita naye limodzi; ndi Akereri ndi Apeleti, ndi Agiti onse, anthu mazana asanu ndi limodzi omtsata kucokera ku Gati, anapita pamaso pa mfumu.
Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 15
Onani 2 Samueli 15:18 nkhani